Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Afilisitiwo anafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo+ kuti amenyane ndi Aisiraeli. Nkhondoyo sinawayendere bwino Aisiraeli, moti anagonjetsedwa ndi Afilisiti.+ Iwo anakantha amuna achiisiraeli pafupifupi 4,000 nkhondoyo ili mkati.

  • 1 Samueli 23:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Amuna amene anali kuyenda ndi Davide anamuyankha kuti: “Ngati tikuchita mantha tili mbali ino ya Yuda,+ ndiye kuli bwanji tikapita ku Keila kukamenyana ndi asilikali a Afilisiti!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena