Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ana a Isiraeli sadzathanso kulimbana ndi adani awo.+ Iwo azingothawa kwa adani awo, chifukwa iwonso akhala zinthu zoyenera kuwonongedwa. Sindidzakhalanso nanu kufikira mutachotsa pakati panu zinthu zoyenera kuwonongedwazo.+

  • Salimo 44:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma tsopano mwatitaya ndi kutichititsa manyazi,+

      Simukuyenda ndi magulu athu ankhondo.+

  • Salimo 79:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pakuti iwo awononga mbadwa zonse za Yakobo,+

      Ndipo malo ake okhalamo awasandutsa bwinja.+

  • Salimo 106:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Mobwerezabwereza anali kuwapereka m’manja mwa anthu a mitundu ina,+

      Kuti anthu odana nawo awalamulire,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena