Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kodi munthu mmodzi angathamangitse bwanji anthu 1,000,

      Kapena anthu awiri angapitikitse bwanji anthu 10,000?+

      N’zosatheka, pokhapokha Thanthwe lawo litawagulitsa,+

      Komanso ngati Yehova atawapereka.

  • Oweruza 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamenepo mkwiyo wa Yehova unayakira Aisiraeli,+ moti anawagulitsa+ kwa Kusani-risataimu, mfumu ya Mesopotamiya.+ Ana a Isiraeli anatumikira Kusani-risataimu zaka 8.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena