Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 kuti, ‘Mverani Aisiraeli inu. Lero mukuyandikira adani anu kuti mumenyane nawo. Mitima yanu isachite mantha.+ Musaope ndipo musathawe mwamantha kapena kunjenjemera chifukwa cha iwo,+

  • Salimo 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ngakhale gulu lankhondo litamanga msasa kuti lindiukire,+

      Mtima wanga sudzachita mantha.+

      Ngakhale nkhondo yolimbana ndi ine itayambika,+

      Pameneponso ndidzadalira Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena