Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 14:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kenako anadalitsa Abulamu kuti:

      “Mulungu Wam’mwambamwamba adalitse Abulamu,+

      Iye amene anapanga kumwamba ndi dziko lapansi.+

  • Genesis 47:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Yosefe anabweretsa bambo ake Yakobo n’kuwasonyeza kwa Farao. Ndipo Yakobo anadalitsa Farao.+

  • Yoswa 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Atatero, Yoswa anawadalitsa+ n’kuwauza kuti azipita kumahema awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena