Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Samueli ndi Sauli anadzuka m’mawa kwambiri, m’bandakucha, ndipo Samueli, ali padenga la nyumba, anaitana Sauli ndi kumuuza kuti: “Konzekera ulendo.” Pamenepo Sauli ananyamuka ndipo onse awiri, iyeyo ndi Samueli, anatuluka kupita panja.

  • Machitidwe 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsiku lotsatira, ulendo wawo uli mkati komanso akuyandikira mzindawo, Petulo anakwera padenga*+ kukapemphera cha m’ma 12 koloko masana.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena