Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Yairi+ mwana wamwamuna wa Manase anatenga dera lonse la Arigobi+ mpaka kumalire a Agesuri+ ndi a Amaakati,+ ndipo midzi ya ku Basana imeneyo anaitcha dzina la iye mwini lakuti, Havoti-yairi*+ kufikira lero.

  • 2 Samueli 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mwana wake wachiwiri anali Kileyabu+ wobadwa kwa Abigayeli+ wa ku Karimeli, amene anali mkazi wa Nabala, ndipo wachitatu anali Abisalomu+ wobadwa kwa Maaka, mwana wamkazi wa Talimai+ mfumu ya ku Gesuri.

  • 2 Samueli 13:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Koma Abisalomu anathawa ndi kupita kwa Talimai,+ mfumu ya dziko la Gesuri,+ amene anali mwana wamwamuna wa Amihudi. Davide anali kulira+ tsiku ndi tsiku chifukwa cha imfa ya Aminoni mwana wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena