Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Inu Yehova, n’chifukwa chiyani adani anga achuluka chotere?+

      N’chifukwa chiyani anthu ondiukira achuluka?+

  • Salimo 43:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Ndiweruzeni+ inu Mulungu,

      Weruzani mlandu wanga+ motsutsana ndi mtundu wosakhulupirika.

      Ndipulumutseni kwa munthu wachinyengo ndi wochita zosalungama.+

  • Miyambo 24:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mwana wanga uziopa Yehova ndiponso mfumu.+ Usamakhale pagulu la anthu ofuna kuti zinthu zisinthe,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena