Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yosiya atatembenuka, anaona manda amene anali m’phirimo. Choncho anatumiza anthu kuti akatenge mafupa m’mandawo, ndipo anawatentha+ paguwa lansembelo kuti alisandutse losayenera kulambirapo, mogwirizana ndi mawu a Yehova+ amene munthu wa Mulungu woona uja, amene analengeza+ zinthu zimenezi, ananena.

  • 2 Mbiri 34:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mafupa+ a ansembe anawatentha pamaguwa awo ansembe.+ Choncho Yosiya anayeretsa Yuda ndi Yerusalemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena