5 dziko la Agebala+ ndiponso dziko lonse la Lebanoni, kotulukira dzuwa, kuyambira ku Baala-gadi+ m’munsi mwa phiri la Herimoni mpaka kumalire ndi Hamati.+
9 Amuna achikulire a ku Gebala+ ndi anthu ake aluso anali mkati mwako monga anthu omata molumikizira matabwa ako.+ Zombo zonse zapanyanja ndi oziyendetsa anali mwa iwe kuti muchite malonda ndi kusinthana zinthu.