Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anamanga zipinda zam’mbali+ zosanjikizana kuzungulira nyumba yonseyo. Chipinda chilichonse chinali chotalika mikono isanu. Zipindazo anazilumikiza kunyumbayo ndi matabwa+ a mkungudza.

  • Ezekieli 41:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anayezanso kuchindikala kwa khoma la nyumbayo ndipo anapeza kuti linali mikono 6. M’lifupi mwa chipinda cham’mbali munali mikono inayi. Umu ndi mmene zinalili kuzungulira nyumba yonseyo.+

  • Ezekieli 41:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 M’mbali mwa khoma la pakhonde, m’zipinda zam’mbali za nyumbayo ndi pamzere wa matabwawo, munali mawindo a mafelemu aakulu mkati koma aang’ono kunja,+ ndipo anajambulamo zithunzi za mtengo wa kanjedza mbali zonse. Zithunzizi anazijambula mochita kugoba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena