Oweruza 8:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Gidiyoni anakhala ndi ana 70+ otuluka m’chiuno mwake, chifukwa anadzakhala ndi akazi ambiri. Oweruza 12:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Iye anabereka ana aamuna 40 ndipo anali ndi zidzukulu 30. Onsewa anali kuyenda pa abulu 70.+ Ndipo Abidoni anaweruza Isiraeli zaka 8.
14 Iye anabereka ana aamuna 40 ndipo anali ndi zidzukulu 30. Onsewa anali kuyenda pa abulu 70.+ Ndipo Abidoni anaweruza Isiraeli zaka 8.