Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chotero iye anapita kukaonekera kwa Asa n’kumuuza kuti: “Tamverani mfumu Asa ndi anthu onse a fuko la Yuda ndi Benjamini. Yehova akhala nanu inuyo mukapitiriza kukhala naye.+ Mukamufunafuna+ iye adzalola kuti mum’peze, koma mukamusiya nayenso adzakusiyani.+

  • Ezara 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndinatero pakuti ndinachita manyazi kupempha kwa mfumu gulu lankhondo+ ndi okwera pamahatchi+ kuti atithandize kumenyana ndi adani m’njira, chifukwa tinali titauza mfumuyo kuti: “Dzanja+ la Mulungu wathu lili ndi onse om’funafuna kuti awachitire zabwino,+ koma mkwiyo wake+ wamphamvu umayakira onse omusiya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena