2 Samueli 3:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Mwana wake wachiwiri anali Kileyabu+ wobadwa kwa Abigayeli+ wa ku Karimeli, amene anali mkazi wa Nabala, ndipo wachitatu anali Abisalomu+ wobadwa kwa Maaka, mwana wamkazi wa Talimai+ mfumu ya ku Gesuri. 2 Samueli 13:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Chotero Abisalomu anathawa ndi kupita ku Gesuri+ ndipo anakhala kumeneko zaka zitatu.
3 Mwana wake wachiwiri anali Kileyabu+ wobadwa kwa Abigayeli+ wa ku Karimeli, amene anali mkazi wa Nabala, ndipo wachitatu anali Abisalomu+ wobadwa kwa Maaka, mwana wamkazi wa Talimai+ mfumu ya ku Gesuri.