Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 5:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano awa ndiwo atsogoleri a nyumba ya makolo awo: Eferi, Isi, Elieli, Azirieli, Yeremiya, Hodaviya, ndi Yahadieli. Onsewa anali atsogoleri a nyumba ya makolo awo, amuna amphamvu, olimba mtima, ndiponso otchuka.

  • 1 Mbiri 11:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano otsatirawa ndiwo atsogoleri a amuna amphamvu+ a Davide omwe anali kulimbikitsa nawo ufumu wake mwamphamvu pamodzi ndi Aisiraeli onse, kuti iye akhale mfumu malinga ndi mawu a Yehova+ okhudza Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena