Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Yehova anali atauza Ahiya kuti: “Kukubwera mkazi wa Yerobowamu kudzakufunsa za mwana wake, chifukwa mwanayo akudwala. Umuuze zakutizakuti. Zomwe zichitike n’zakuti, akangofika adzisintha kuti asadziwike.”+

  • 1 Mafumu 20:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Kenako, mneneriyo anakaima m’mphepete mwa msewu n’kumakadikirira mfumu ija, atadzimanga kansalu kumaso kuti asadziwike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena