Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Inu Mulungu wanga, ine ndikudziwa bwino kuti inu ndinu wosanthula mitima,+ ndiponso kuti mumakonda chilungamo.+ Ineyo kumbali yanga, ndapereka zinthu zonsezi mwaufulu ndi mtima wowongoka. Ndasangalala kuona anthu anu ali apawa, akupereka zopereka zawo mwaufulu kwa inu.

  • Salimo 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chishango changa chili ndi Mulungu,+ Mpulumutsi wa anthu owongoka mtima.+

  • Salimo 94:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pakuti zigamulo zidzayambiranso kukhala zachilungamo,+

      Ndipo onse owongoka mtima adzazitsatira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena