Ekisodo 29:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Uzipereka mwana wa nkhosa mmodzi m’mawa,+ ndipo mwana wa nkhosa winayo madzulo kuli kachisisira.*+ Numeri 28:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Mwana wa nkhosa mmodzi wamphongo muzim’pereka nsembe m’mawa. Ndipo mwana wa nkhosa wamphongo winayo, muzim’pereka nsembe madzulo kuli kachisisira.*+
39 Uzipereka mwana wa nkhosa mmodzi m’mawa,+ ndipo mwana wa nkhosa winayo madzulo kuli kachisisira.*+
4 Mwana wa nkhosa mmodzi wamphongo muzim’pereka nsembe m’mawa. Ndipo mwana wa nkhosa wamphongo winayo, muzim’pereka nsembe madzulo kuli kachisisira.*+