Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho Hezekiya mfumu ya Yuda anatumiza uthenga kwa mfumu ya Asuri ku Lakisi, wakuti: “Ndachimwa. Siyani kundiukira. Ndikupatsani chilichonse chimene mungandilamule.”+ Chotero mfumu ya Asuri inalamula Hezekiya mfumu ya Yuda kuti apereke matalente* 300 a siliva+ ndi matalente 30 a golide.

  • 2 Mbiri 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Yotamu anamenyana ndi mfumu ya ana a Amoni+ ndipo pomalizira pake anawaposa mphamvu. Choncho chaka chimenecho ana a Amoni anam’patsa matalente a siliva* 100 ndi tirigu+ wokwana miyezo 10,000 ya kori,*+ komanso balere wokwana miyezo 10,000 ya kori.+ Izi n’zimene ana a Amoni anamulipira. Anamulipiranso zomwezi m’chaka chachiwiri ndi chachitatu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena