Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Imvani dandaulo lolungama, inu Yehova. Mvetserani kulira kwanga kochonderera.+

      Tcherani khutu ku pemphero langa limene likutuluka pamilomo yopanda chinyengo.+

  • Salimo 31:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Tcherani khutu lanu kwa ine.+

      Ndilanditseni mofulumira.+

      Mukhale thanthwe lolimba kwa ine,+

      Mukhale nyumba ya mpanda wolimba kuti mundipulumutse.+

  • Salimo 65:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Inu Wakumva pemphero, anthu a mitundu yonse adzabwera kwa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena