Ekisodo 23:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “Katatu pa chaka muzindichitira chikondwerero.+ Levitiko 23:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 “‘Zikondwerero+ za Yehova, kapena kuti misonkhano yopatulika+ imene muyenera kulengeza pa nthawi yake yoikidwiratu+ ndi iyi:
4 “‘Zikondwerero+ za Yehova, kapena kuti misonkhano yopatulika+ imene muyenera kulengeza pa nthawi yake yoikidwiratu+ ndi iyi: