Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Aamoni+ anayamba kupereka msonkho+ kwa Uziya. Pomalizira pake, kutchuka kwake+ kunafika mpaka ku Iguputo chifukwa anasonyeza mphamvu zochuluka zedi.

  • Yobu 42:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Abale ake onse, alongo ake onse ndi onse amene anali kumudziwa kale+ ankabwera kwa iye. Iwo anayamba kudyera naye pamodzi mkate+ m’nyumba mwake, komanso anali kumulimbikitsa ndi kum’pepesa chifukwa cha tsoka lonse limene Yehova analola kuti lim’gwere. Aliyense wa iwo anapatsa Yobu mphatso ya ndalama ndi mphete yagolide.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena