Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno anthu onse anasonkhana pamodzi mogwirizana+ m’bwalo lalikulu+ limene linali pafupi ndi Chipata cha Kumadzi.+ Pamenepo anthuwo anauza Ezara+ wokopera Malemba kuti abweretse buku+ la chilamulo cha Mose+ limene Yehova analamula Aisiraeli kuti azilitsatira.+

  • Nehemiya 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ezara wokopera Malembayo, anaimirira pansanja yamatabwa+ imene inamangidwa chifukwa cha mwambo umenewu. Pafupi naye, kudzanja lake lamanja kunaimirira Matitiya, Sema, Anaya, Uriya, Hilikiya, ndi Maaseya. Ndipo kudzanja lake lamanzere kunaimirira Pedaya, Misayeli, Malikiya,+ Hasumu,+ Hasi-badana, Zekariya ndi Mesulamu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena