-
Yeremiya 35:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Onsewa ndinawabweretsa m’nyumba ya Yehova. Ndinalowa nawo m’chipinda chodyera+ cha ana a Hanani mwana wa Igadaliya, munthu wa Mulungu woona. Chipinda chimenechi chinali pafupi ndi chipinda chodyera cha akalonga chimene chinali pamwamba pa chipinda chodyera cha Maaseya mwana wa Salumu,+ amene anali mlonda wa pakhomo.
-