Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 8:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Antchito anu aamuna, antchito anu aakazi, abusa anu aluso kwambiri ndi abulu anu idzawatenganso kuti ikawagwiritse ntchito.+

  • 2 Samueli 16:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno mfumu inafunsa Ziba kuti: “Kodi zinthu zimene watengazi n’zachiyani?”+ Poyankha Ziba anati: “Abuluwa ndatengera anthu a m’nyumba ya mfumu kuti azikwerapo, mkate ndi makeke a zipatso za m’chilimwe ndatengera anyamata+ kuti adye, ndipo vinyo ndatengera munthu wotopa+ m’chipululu+ kuti amwe.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena