Ekisodo 16:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Dziwani kuti Yehova wakupatsani sabata.+ N’chifukwa chake akukupatsani mkate wa masiku awiri pa tsiku la 6. Pa tsiku la 7 aliyense azikhala pamalo ake.+ Munthu asachoke pamalo ake.” Ekisodo 20:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma tsiku la 7 ndi sabata la Yehova Mulungu wanu.+ Musagwire ntchito iliyonse inuyo kapena mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, chiweto chanu kapena mlendo wokhala mumzinda wanu.+ Deuteronomo 5:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “‘Posunga tsiku la sabata ndi kuliona kukhala lopatulika, mmene Yehova Mulungu wako anakulamulira,+
29 Dziwani kuti Yehova wakupatsani sabata.+ N’chifukwa chake akukupatsani mkate wa masiku awiri pa tsiku la 6. Pa tsiku la 7 aliyense azikhala pamalo ake.+ Munthu asachoke pamalo ake.”
10 Koma tsiku la 7 ndi sabata la Yehova Mulungu wanu.+ Musagwire ntchito iliyonse inuyo kapena mwana wanu wamwamuna, mwana wanu wamkazi, kapolo wanu wamwamuna, kapolo wanu wamkazi, chiweto chanu kapena mlendo wokhala mumzinda wanu.+
12 “‘Posunga tsiku la sabata ndi kuliona kukhala lopatulika, mmene Yehova Mulungu wako anakulamulira,+