Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsopano vomerezani+ machimo anu kwa Yehova Mulungu wa makolo anu, ndipo chitani zomusangalatsa+ ndi kudzipatula kwa anthu a mitundu ina ndiponso kwa akazi achilendo.”+

  • Nehemiya 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamenepo mbewu ya Isiraeli inadzipatula+ kwa anthu onse osakhala Aisiraeli.+ Atatero anaimirira ndi kuulula+ machimo awo+ ndi zolakwa za makolo awo.+

  • Nehemiya 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndiyeno anthu ena onse, ansembe,+ Alevi,+ alonda a pazipata,+ oimba,+ Anetini,+ ndi aliyense amene anadzipatula kwa mitundu ya anthu a m’mayikowo+ kuti asunge chilamulo+ cha Mulungu woona, akazi awo, ana awo aamuna ndi ana awo aakazi ndi aliyense wodziwa zinthu ndi wozindikira,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena