Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 36:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungutu ndi wamphamvu+ ndipo sadzakana munthu.

      Iye ali ndi mphamvu zazikulu zomvetsa zinthu.

  • Salimo 104:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ntchito zanu ndi zochuluka, inu Yehova!+

      Zonsezo munazipanga mwanzeru zanu.+

      Dziko lapansi ladzaza ndi zinthu zimene munapanga.+

  • Yesaya 40:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Kwezani maso anu kumwamba muone. Kodi ndani amene analenga zinthu zimenezo?+ Ndi amene akutsogolera gulu lonse la nyenyezizo malinga ndi chiwerengero chake, ndipo amaziitana potchula iliyonse dzina lake.+ Chifukwa cha kuchuluka kwa mphamvu zake zoopsa,+ ndiponso chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zambiri zochitira zinthu, palibe imene imasowa.

  • Danieli 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iye anati: “Dzina la Mulungu likhale lotamandika+ kuyambira kalekale mpaka kalekale, pakuti nzeru ndi mphamvu ndi zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena