Salimo 35:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Anthu ampatuko amene anali kunditonza kuti apeze kachakudya,+Anandikukutira mano.+ Aheberi 11:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Ena analandira mayesero awo mwa kutonzedwa ndi kukwapulidwa, komanso kuposa pamenepo, mwa maunyolo+ ndi ndende.+
36 Ena analandira mayesero awo mwa kutonzedwa ndi kukwapulidwa, komanso kuposa pamenepo, mwa maunyolo+ ndi ndende.+