Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mulungu si munthu, woti anganene mabodza,+

      Si mwana wa munthu, woti angadzimve kuti ali ndi mlandu.+

      Kodi ananenapo kanthu koma osachita,

      Analankhulapo kanthu kodi koma osakwaniritsa?+

  • Numeri 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Inetu ndalamulidwa kudzadalitsa,

      Ndipo Iye wadalitsa,+ ine sindisintha zimenezo.+

  • Aroma 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mwina unganene kwa ine kuti: “N’chifukwa chiyani Mulungu akupezabe anthu zifukwa? Kodi ndani angatsutse chifuniro chake chimene chinanenedwa?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena