Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Masana Yehova adzalamula kukoma mtima kwake kosatha kuti kufike pa ine,+

      Ndipo usiku ndidzaimba za iye.+

      Ndidzapemphera kwa Mulungu wondipatsa moyo.+

  • Salimo 77:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Usiku ndidzakumbukira nyimbo zanga zoimbidwa ndi chipangizo cha zingwe.+

      Ndidzasonyeza kudera nkhawa mumtima mwanga,+

      Ndipo ndidzasinkhasinkha zinthu zonse mozama.

  • Salimo 149:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Anthu okhulupirika akondwere mu ulemerero.

      Iwo aimbe mosangalala pamabedi awo.+

  • Machitidwe 16:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma chapakati pa usiku,+ Paulo ndi Sila anali kupemphera ndi kutamanda Mulungu poimba nyimbo,+ ndipo akaidi ena anali kuwamva.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena