Salimo 84:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Inu Yehova wa makamu, wodala ndi munthu amene amakhulupirira inu.+ Salimo 94:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Koma Yehova adzakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+Ndipo Mulungu wanga adzakhala thanthwe langa lothawirako.+
22 Koma Yehova adzakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+Ndipo Mulungu wanga adzakhala thanthwe langa lothawirako.+