Salimo 55:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Mtima wanga ukundipweteka kwambiri.+Ndipo ndikuopa imfa.+ Maliko 14:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Ndiyeno anawauza kuti: “Moyo wanga ukumva chisoni chofa nacho.+ Khalani pompano ndipo mukhalebe maso.”+
34 Ndiyeno anawauza kuti: “Moyo wanga ukumva chisoni chofa nacho.+ Khalani pompano ndipo mukhalebe maso.”+