Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 29:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pamene anachititsa nyale yake kuwala pamutu panga,

      Pamene ndinkayenda mu mdima iye akundiunikira ndi kuwala kwake.+

  • Salimo 40:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, musasiye kundimvera chisoni.+

      Kukoma mtima kwanu kosatha komanso choonadi chanu zinditeteze nthawi zonse.+

  • Miyambo 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti lamulolo ndilo nyale,+ ndipo malangizo ndiwo kuwala,+ komanso kudzudzula* kowongola zolakwa ndiko njira yamoyo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena