Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 48:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Taonani! Mafumu anakumana atapangana,+

      Koma anangodutsa.+

  • Luka 13:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Mu ola lomwelo kunafika Afarisi ena ndi kumuuza kuti: “Nyamukani muchoke kuno, chifukwa Herode* akufuna kukuphani.”

  • Luka 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo Herode pamodzi ndi asilikali ake omulondera anamupeputsa.+ Anamuchitira zachipongwe+ mwa kumuveka chovala chonyezimira ndipo anamutumizanso kwa Pilato.

  • Chivumbulutso 19:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo ndinaona chilombo,+ mafumu+ a dziko lapansi, ndi magulu awo ankhondo atasonkhana pamodzi kuti amenyane+ ndi wokwera pahatchi+ uja ndi gulu lake lankhondo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena