Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Tsiku lonse adani anga akufuna kundiwakha ndi pakamwa pawo,+

      Pakuti anthu ambiri akumenyana nane modzikuza.+

  • Ezekieli 36:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Choncho losera ndipo unene kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Inu mwakhala bwinja+ ndipo adani anu akulumani kumbali zonse.+ Izi zachitika kuti anthu otsala a mitundu ina akutengeni kuti mukhale awo.+ Anthu akunena za inu ndi pakamwa pawo+ ndipo akukunenerani zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena