Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pakuti aliyense wodya mafuta a nyama imene waipereka kwa Yehova monga nsembe yotentha ndi moto, munthu ameneyo aziphedwa+ kuti asakhalenso pakati pa anthu a mtundu wake.

  • Salimo 36:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amadya ndi kukhuta chakudya chonona m’nyumba mwanu.+

      Ndipo mumawamwetsa mumtsinje wa zosangalatsa zanu zambiri.+

  • Yeremiya 31:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ansembe ndidzawatsitsimutsa ndi chakudya chochuluka,+ ndipo anthu anga ndidzawakhutiritsa ndi ubwino wanga,”+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena