Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pa chifukwa chimenechi, aliyense wokhulupirika adzapemphera kwa inu,+

      Pa nthawi imene inu mungapezeke.+

      Ndipo madzi ambiri osefukira sadzamukhudza ngakhale pang’ono.+

  • Yona 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pamene munandiponya m’malo ozama, pansi penipeni pa nyanja yakuya,+

      Madzi amphamvu anandimiza.

      Mafunde anu amphamvu anadutsa pamwamba panga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena