Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Tsopano Yehova wanena kuti: “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa osautsika, chifukwa cha kuusa moyo kwa anthu osauka,+

      Ndidzanyamuka pa nthawiyo,+

      Ndidzawateteza kwa aliyense wowanyodola.”+

  • Salimo 72:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Aweruze osautsika pakati pa anthu,+

      Apulumutse ana a anthu osauka,

      Ndipo aphwanye wobera anzake mwachinyengo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena