Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 (Eli anali ndi zaka 98, ndipo maso ake anangokhala tong’o koma sanali kuona.)+

  • Salimo 37:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinali mwana, ndipo tsopano ndakula,+

      Koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa,+

      Kapena ana ake akupemphapempha chakudya.+

  • Salimo 71:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Musanditaye nthawi ya ukalamba wanga.+

      Musandisiye pa nthawi imene mphamvu zanga zikutha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena