Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndikuikiza mzimu* wanga m’manja mwanu.+

      Mwandiwombola,+ inu Yehova, Mulungu wachoonadi.+

  • Salimo 130:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Isiraeli ayembekezere Yehova,+

      Pakuti Yehova amasonyeza kukoma mtima kosatha.+

      Iye ali ndi mphamvu zochuluka zowombolera anthu ake.+

  • Salimo 145:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova ndi wachisomo ndi wachifundo,+

      Wosakwiya msanga ndi wosonyeza kukoma mtima kosatha komanso kwakukulu.+

  • Yoweli 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ng’ambani mitima yanu+ osati zovala zanu+ ndipo bwererani kwa Yehova Mulungu wanu pakuti iye ndi wachisomo, wachifundo,+ wosakwiya msanga+ ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha.+ Ndithu, iye adzakumverani chisoni chifukwa cha tsokalo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena