Salimo 6:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndalefuka chifukwa cha kuusa moyo* kwanga.+Usiku wonse ndimanyowetsa bedi langa.+Ndimakhathamitsa bedi langa ndi misozi.+ Salimo 38:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ndalefuka ndipo ndaponderezeka kwambiri.Ndikulira mofuula chifukwa cha kuvutika kwa mtima wanga.+
6 Ndalefuka chifukwa cha kuusa moyo* kwanga.+Usiku wonse ndimanyowetsa bedi langa.+Ndimakhathamitsa bedi langa ndi misozi.+