-
2 Samueli 13:36Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
36 Ndiyeno atangomaliza kulankhula, ana a mfumu aja anafika ndipo anayamba kulira mokweza mawu. Mfumu nayonso pamodzi ndi atumiki ake onse analira kwadzaoneni.
-