Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 22:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mikaya anapitiriza kunena kuti: “Choncho imvani mawu a Yehova:+ Ndinaona Yehova atakhala pampando wake wachifumu,+ makamu onse akumwamba ataimirira kudzanja lake lamanja ndi kumanzere kwake.+

  • Salimo 148:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mutamandeni, inu angelo ake onse.+

      Mutamandeni, inu khamu lake lonse.+

  • Yesaya 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Choncho mawu a Ambuye woona, Yehova wa makamu, Wamphamvu wa Isiraeli,+ ndi akuti: “Eya! Ndidzibweretsera mpumulo pochotsa adani anga ndipo ndibwezera+ odana nane.+

  • Luka 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwadzidzidzi, panaoneka khamu lalikulu lakumwamba+ pamodzi ndi mngeloyo, likutamanda Mulungu+ kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena