Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ana onse a Isiraeli anayamba kudandaula za Mose ndi Aroni.+ Ndipo khamu lonselo linati: “Zikanakhala bwino tikanangofera ku Iguputo, kapena tikanangofera m’chipululu muno.

  • Numeri 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Kodi khamu la anthu oipa amenewa lidandaula motsutsana nane kufikira liti?+ Ndamva kudandaula konseko kumene ana a Isiraeli akuchita motsutsana nane.+

  • Deuteronomo 1:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamenepo munapitiriza kung’ung’udza m’mahema mwanu kuti, ‘Yehova anatitulutsa m’dziko la Iguputo+ chifukwa chodana nafe,+ kuti adzatipereke m’manja mwa Aamori kuti atiwononge.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena