Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa cha dzina lanu, inu Yehova,+

      Mundikhululukire cholakwa changa ngakhale kuti n’chachikulu.+

  • Salimo 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti inu ndinu thanthwe langa ndi malo anga achitetezo.+

      Chifukwa cha dzina lanu+ mudzanditsogolera ndi kundilozera njira.+

  • Yohane 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Komanso, ine sindikhalanso m’dzikoli pakuti ndikubwera kwa inu, koma iwo adakali m’dzikoli.+ Atate Woyera, ayang’anireni+ chifukwa cha dzina lanu limene mwandipatsa, kuti akhale amodzi mmene ife tilili.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena