Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Aiguputo+ anenerenji kuti, ‘Anawatulutsa m’dziko lino kuti akawaphe kumapiri ndi kuwafafaniza padziko lapansi’?+ Bwezani mkwiyo wanu woyaka motowo,+ ndipo mverani chisoni+ anthu anu kuti musawagwetsere tsoka.

  • Numeri 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mukapha anthuwa kamodzi n’kamodzi ngati mukupha munthu mmodzi,+ ndithu mitundu imene yamva za ukulu wanu idzati,

  • Deuteronomo 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ngati ndikanati sindikuopa kusautsidwa ndi mdani,+

      Kuti adani awo angamve molakwa,+

      Kutinso anganene kuti: “Dzanja lathu lapambana,+

      Ndipo si Yehova amene wachita zonsezi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena