Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Wodala ndi munthu wamphamvu amene amakhulupirira Yehova,+

      Munthu amene sanacheukire anthu otsutsa,

      Kapena anthu amene anapatukira m’njira za mabodza.+

  • Salimo 62:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mukhulupirireni nthawi zonse, anthu inu.+

      Mukhuthulireni za mumtima mwanu.+

      Mulungu ndiye pothawirapo pathu.+ [Seʹlah.]

  • Yeremiya 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Yehova wanena kuti: “Wotembereredwa ndi munthu aliyense wokhulupirira mwa munthu aliyense wochokera kufumbi.+ Wotembereredwa ndi munthu amene amadalira mphamvu za dzanja la munthu,+ komanso amene mtima wake wapatuka kuchoka kwa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena