Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:97
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  97 Ndimakonda kwambiri chilamulo chanu!+

      Ndimasinkhasinkha chilamulocho tsiku lonse.+

  • Salimo 128:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 128 Wodala ndi aliyense woopa Yehova,+

      Amene amayenda m’njira za Mulungu.+

  • Aroma 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mumtima mwanga+ ndimasangalala kwambiri+ ndi chilamulo cha Mulungu,

  • Yakobo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma woyang’anitsitsa m’lamulo langwiro+ limene limabweretsa ufulu, amene amalimbikira kutero, adzakhala wosangalala+ polichita chifukwa chakuti sali wongomva n’kuiwala, koma wochita.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena