Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Alozetse mtima wathu+ kwa iye kuti tiyende m’njira zake zonse+ ndi kusunga malamulo ake,+ malangizo ake,+ ndi zigamulo zake,+ zimene analamula makolo athu.

  • Salimo 119:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  33 Ndilangizeni inu Yehova, kuti ndiyende motsatira malangizo anu,+

      Kuti nditsatire malangizo anu moyo wanga wonse.+

  • Salimo 119:124
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 124 Ndichitireni zabwino ine mtumiki wanu monga mwa kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Ndipo ndiphunzitseni malamulo anu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena